Chidziwitso cha Matenda a Mthomba ya Nkhuku (Chikwirikwiti)

Matenda awa amapezeka kwambiri muno m'Malawi. Ndipo amafala kuchokera ku nkhuku zodwala pamene zakhudzana ndi zamoyo.

fowl-pox-01.jpg    fowl-pox-02.jpg
Photo: Trufosa Phiri
(Facebook - Local Chicken Farmers in Malawi)

Maonekedwe a Matendawa

  • Zizindikiro: Tizilonda totupa pa lipombo ndi m'matende. Nthawi zina timaoneka pali ponse pa mutu.
  • Nkhuku imadwala matendawa kwa sabata limodzi, nkhuku zina zitha kufa ndi matendawa.

Choyambitsa

  • Kachirombo kamtundu wa virus kamene kamapezeka kwambiri muno m'Malawi.

Kuchiza

  • Palibe mankhwala ochiza matendawa. Ngati matenda agwa m'khola, amatha okha.
  • Koma kupaka mankhwala a iodine pa tizilonda kumathandiza kuchira.

Kuteteza

  • Kuli katemera amene amapezeka ku veterinary shops. Katemerayu amateteza matendawa ngati sanagwe m'khola.




pic07_20181113_101534_85pc240px.jpg
A little story
about our impact


logo-tropical-water-solutions.png
What is TWS?


pic20170818_102628-225.jpg
How an Australian vaccine is helping rural communities in Africa.
Celia Grenning explains.


Facebook